LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 17
  • ‘Nifuna’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Nifuna’
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Ndikufuna”
    Imbirani Yehova
  • Cikondi ca Umulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Chizindikiro cha Ophunzira a Khristu
    Imbirani Yehova
  • Cikondi Khalidwe Lamtengo Wapatali
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 17

NYIMBO 17

‘Nifuna’

Yopulinta

(Luka 5:13)

  1. 1. Mwana wa Yehova M’lungu,

    Anaonetsa cikondi.

    Pobwela padziko Kutithandiza;

    Iye anadzipeleka.

    Anacilitsa

    odwala,

    Ogontha na osaona.

    Nchito yake anakwanilitsa

    Iye anati: ‘Nifuna.’

  2. 2. Tiyesetse kutengela,

    Yesu mu umoyo wathu.

    Pophunzitsa anthu, Kudziŵa M’lungu;

    Tikhale okoma mtima.

    Tithandize anthu onse,

    Akasoŵa zilizonse.

    Conco amasiye akapempha

    Tiyankhe kuti: ‘Nifuna.’

(Onaninso Yoh. 18:37; Aef. 3:19; Afil. 2:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani