LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 103
  • Abusa ni Mphatso za Amuna

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Abusa ni Mphatso za Amuna
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna
    Imbirani Yehova
  • Khulupilila Coonadi Iwe Mwini
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 103

NYIMBO 103

Abusa ni Mphatso za Amuna

Yopulinta

(Aefeso 4:8)

  1. 1. Yehova ‘tipatsa Abusa,

    Kuti atiwete.

    Mwa citsanzo cawo cabwino,

    Amatsogolela.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa amuna,

    Amatisamalila.

    Iwo ni okhulupilika;

    Ise tiziŵakonda.

  2. 2. Abusawa amatikonda;

    Amatisamala.

    Tikavulala mwauzimu,

    Amaticilitsa.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa amuna,

    Amatisamalila.

    Iwo ni okhulupilika;

    Ise tiziŵakonda.

  3. 3. Kuti ise tisatayike,

    Amatilangiza.

    Amatithandiza kuyenda,

    M’njila ya Yehova.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa amuna,

    Amatisamalila.

    Iwo ni okhulupilika;

    Ise tiziŵakonda.

(Onaninso Yes. 32:1, 2; Yer. 3:15; Yoh. 21:15-17; Mac. 20:28.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani