LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 88
  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ana ni Mphatso Zimene Mulungu Amaikiza kwa Makolo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • N’zotheka Kuti Muziwadalila Abale Anu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Abusa ni Mphatso za Amuna
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 88

Nyimbo 88

Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

(Salimo 127:3-5)

1. Mwamuna ’kakhala bambo,

Mkazinso akakhala ndi mwana.

Afunika akumbukire,

Mwanayo siwawo okha.

Ndi mphatso yochoka kwa M’lungu

Amapatsa chikondi ndi moyo.

Amapatsanso malangizo

Othandizadi kwa makolo.

(KOLASI)

Mphatso yanu njopatulika

Ndipo muisamalire.

M’phunzitseni mwana cho’nadi

Choncho mungamuthandize.

2. Malamulo ’nse a M’lungu

Muziwasunga mumtima mwanu.

Muziphunzitsa ana anu,

Uwu ndi udindo wanu.

Muziwaphunzitsa poyenda,

Podzuka ndi pa nthawi yopuma.

Choncho iwo sadzaiwala

Adzakhala odalitsidwa.

(KOLASI)

Mphatso yanu njopatulika

Ndipo muisamalire.

M’phunzitseni mwana cho’nadi

Choncho mungamuthandize.

(Onaninso Deut. 6:6, 7; Aef. 6:4; 1 Tim. 4:16.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani