LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 65
  • “Njira ndi Iyi”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Njira ndi Iyi”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Njila ni Iyi”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Abusa ni Mphatso za Amuna
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 65

Nyimbo 65

“Njira ndi Iyi”

(Yesaya 30:20, 21)

1. Pali njira imene

Munaidziwa,

Njira yamtendere

Munaiphunzira

Pamene munamvera

Mawu a Yesu,

Ndi njira yopezeka

M’mawu a M’lungu.

(KOLASI)

Njira yakumoyo ndi ’meneyi

M’sacheuke m’sapite kumbali

Mawu a Mulungu akuti,

‘M’sapatuke njira ndi ’meneyi.’

2. Pali njira imene

Ndi yachikondi,

Tikaitsatira

Timaona kuti

Chikondi cha Mulungu

Ndi chochuluka,

Njirayi yachikondi

Imatikhudza.

(KOLASI)

Njira yakumoyo ndi ’meneyi

M’sacheuke m’sapite kumbali

Mawu a Mulungu akuti,

‘M’sapatuke njira ndi ’meneyi.’

3. Pali njira ya moyo

Imodzi yokha,

Palibe inanso

M’lungu walonjeza,

Ndi yokhayi

Tingapezemo chikondi,

Njira yakumoyotu

Ndi imeneyi.

(KOLASI)

Njira yakumoyo ndi ’meneyi

M’sacheuke m’sapite kumbali

Mawu a Mulungu akuti,

‘M’sapatuke njira ndi ’meneyi.’

(Onaninso Sal. 32:8; 139:24; Miy. 6:23.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani