LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 30
  • Tate Wanga, Mulungu Wanga, Bwenzi Langa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tate Wanga, Mulungu Wanga, Bwenzi Langa
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa
    Imbirani Yehova
  • Dzina Lanu Ndimwe Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 30

NYIMBO 30

Tate Wanga, Mulungu Wanga, Bwenzi Langa

Yopulinta

(Aheberi 6:10)

  1. 1. Nthawi zina m’dzikoli,

    Moyo ungakhale wovuta.

    Koma ine nidziŵa

    Moyo ni wabwino.

    (KOLASI)

    Yehova ‘tate wanga, Adziŵa kuti nimukonda.

    Iye sadzanisiya; Ndipo sadzaniiŵala.

    Ngakhale nivutike Iye adzanisamalila.

    Yehova ni Bwenzi langa, M’lungu wanga.

  2. 2. Tsopano nakalamba;

    Nthawi ya mavuto yafika.

    Koma niyembekeza

    Dziko latsopano.

    (KOLASI)

    Yehova ‘tate wanga, Adziŵa kuti nimukonda.

    Iye sadzanisiya; Ndipo sadzaniiŵala.

    Ngakhale nivutike Iye adzanisamalila.

    Yehova ni Bwenzi langa, M’lungu wanga.

(Onaninso Sal. 71:17, 18.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani