LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 99
  • Abale Miyanda Miyanda

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Abale Miyanda Miyanda
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khamu la Abale
    Imbirani Yehova
  • Zoona Zake Ponena za Angelo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 99

NYIMBO 99

Abale Miyanda Miyanda

Yopulinta

(Chivumbulutso 7:9,10)

  1. 1. Abale ni myanda myanda,

    Osaŵelengeka,

    Aliyense ni mboni,

    Yokhulupilika.

    Ise ndise ambili,

    Tikuwonjezeka,

    Tacoka kumitundu yonse,

    Titamanda M’lungu.

  2. 2. Ise tili myanda myanda,

    Timalalikila

    Za uthenga wabwino,

    Ku mitundu yonse.

    Olo tileme bwanji,

    Timalalikila,

    Yesu amatitsitsimula;

    Timapeza mphamvu.

  3. 3. Abale ni myanda myanda,

    M’lungu atikonda,

    Iye afuna kuti,

    Tizim’tumikila.

    Mokondwa tilengeza,

    Za Ufumu wake,

    Tikagwila nchito na M’lungu,

    Timasangalala.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 11:29; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani