LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 55
  • Musaŵayope!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musaŵayope!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Musawaope!
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 55

NYIMBO 55

Musaŵayope!

Yopulinta

(Mateyu 10:28)

  1. 1. Patsogolo, anthu anga,

    Musayope adani.

    Lalikilani mau,

    Anthu onse adziŵe

    Kuti mwana wanga Khristu

    Lomba alamulila.

    Posacedwa adzamanga

    Satana mdani wathu.

    (KOLASI)

    Musayope, anthu anga,

    Olo akuyofyeni.

    Ine nidzakusungani.

    Sinidzakusiyani.

  2. 2. Ngakhale adani anu,

    Aculuke padziko,

    Olo akuyofyeni,

    Olo akuzunzeni,

    Anthu anga musayope,

    Nidzakutetezani.

    Nidzakusamalilani

    Mpaka mudzapambana.

    (KOLASI)

    Musayope, anthu anga,

    Olo akuyofyeni.

    Ine nidzakusungani.

    Sinidzakusiyani.

  3. 3. Siningakuiŵaleni;

    Nidzakulimbitsani.

    Ngakhale akupheni,

    Nidzakuukitsani.

    Anthu anga khulupilikani

    Mpaka mapeto.

    Ndipo ine nidzakupatsani

    Moyo wosatha.

    (KOLASI)

    Musayope, anthu anga,

    Olo akuyofyeni.

    Ine nidzakusungani.

    Sinidzakusiyani.

(Onaninso Deut. 32:10; Neh. 4:14; Sal. 59:1; 83:2, 3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani