LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 123
  • Gonjelani Dongosolo la Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Gonjelani Dongosolo la Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tizigonjera Mokhulupirika Dongosolo la Mulungu Loyendetsera Zinthu
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 123

NYIMBO 123

Gonjelani Dongosolo la Mulungu

Yopulinta

(1 Akorinto 14:33)

  1. 1. Anthu a Yehova polalikila

    Uthenga wabwino pa dziko lonse,

    Mokhulupilika amatsatila

    Dongosolo lake Yehova M’lungu.

    (KOLASI)

    Tizigonjela Mulungu wathu,

    Mokhulupilika.

    Atiteteza, aticengeta,

    Timukhulupilile.

  2. 2. Atate Yehova anatipatsa

    Kapolo wake na mzimu woyela.

    Amafuna kuti ticilimike,

    Mokhulupilika tim’tumikile!

    (KOLASI)

    Tizigonjela Mulungu wathu,

    Mokhulupilika.

    Atiteteza, aticengeta,

    Timukhulupilile.

(Onaninso Luka 12:42; Aheb. 13:7, 17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani