LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 93
  • Dalitsani Misonkhano Yathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Dalitsani Misonkhano Yathu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • N’cifukwa Ciani Tiyenela Kusonkhana?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 93

NYIMBO 93

Dalitsani Misonkhano Yathu

Yopulinta

(Aheberi 10:24, 25)

  1. 1. Tidalitseni Yehova

    Pamene tisonkhana.

    Timakonda misonkhano;

    Mzimu ukhale nafe.

  2. 2. Tipatseni Mau anu

    Kuti atiyeletse.

    Tilalikile kwa onse;

    Tikhale na Cikondi.

  3. 3. Tidalitseni Yehova;

    Tikhale na mtendele.

    Mau na zocita zathu

    Zikulemekezeni.

(Onaninso Sal. 22:22; 34:3; Yes. 50:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani