LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • g19 na. 3 masa. 14-15
  • Buku Lothandiza Kwambili m’Mbili Yonse ya Anthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Buku Lothandiza Kwambili m’Mbili Yonse ya Anthu
  • Galamuka!—2019
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • KUMASULILA NA KUFALITSIDWA KWA BAIBO
  • DZIŴANI ZAMBILI
  • MABAIBO AMENE AFALITSIDWA NA MBONI ZA YEHOVA
  • BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO
  • Baibo Yakumana na Zambili
    Galamuka!—2007
  • Yehova Mulungu Amakonda Kukamba ndi Anthu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Zida Zogwilitsila Nchito Polalikila—Kusindikiza Mabuku Ogaŵila Padziko Lonse Lapansi
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Baibulo Lomasulidwa Bwino Kwambili
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onaninso Zina
Galamuka!—2019
g19 na. 3 masa. 14-15
Aŵelenga Baibo

Buku Lothandiza Kwambili M’mbili Yonse Ya Anthu

Baibo ni buku imene yamasulilidwa na kufalitsidwa kuposa buku lina lililonse. Conco, nzelu zopezeka m’Baibo zafikila anthu ambili na kuŵathandiza kuposa buku lina lililonse. Onani ziŵelengelo zotsatilazi:

KUMASULILA NA KUFALITSIDWA KWA BAIBO

Mulu wa Mabaibo
  • 96.5 pelesenti ya ciŵelengelo ca anthu pa dziko lonse angakhale na Baibo

  • Ipezeka m’vitundu 3,350 (YATHUNTHU KAPENA MBALI YAKE)

  • MABAIBO 5 BILIYONI Kapena kuposapo apangidwa. M’mbili yonse ya anthu, ici n’ciŵelengelo cacikulu kuposa buku lina lililonse

DZIŴANI ZAMBILI

YENDANI PA WEBUSAITI YATHU YA JW.ORG. PA WEBUSAITI IMENEYI:

  • Mungaŵelenge Baibo (m’vitundu vofika m’mahandiledi)

  • Mungacite daunilodi Baibo

  • Mungapeze mayankho pa mafunso a m’Baibo

  • Mungaŵelenge nkhani za mmene Baibo yathandizila anthu ambili kukhala na umoyo wabwino

  • Mungacite maphunzilo a Baibo a pa intanetia

  • Mungapemphe kuti wina aziphunzila Baibo na imwe

MABAIBO AMENE AFALITSIDWA NA MBONI ZA YEHOVA

MBONI ZA YEHOVA ZAYESETSA KUMASULILA NA KUFALITSA BAIBO.

Ena mwa ma Baibo amene tafalitsa kwa zaka zambili ni awa:

  • American Standard Version ya mu 1901

  • The Bible in Living English, Byington

  • The Emphatic Diaglott

  • King James Version

  • Revised Standard Version

  • Baibo ya Tischendorf ya Cipangano Catsopano

BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO

Chati yoonetsa kuculuka kwa Mabaibulo a Dziko Latsopano amene apangidwa kucokela mu 1950 mpaka 2020
  • Ili m’vitundu vopitilila 180 (YATHUNTHU KAPENA MBALI YAKE)

  • 227 MILIYONI MABAIBO A DZIKO LATSOPANO AMENE APULINTIWA KUCOKELA MU 1950

a Palipano, maphunzilo amenewa apezeka cabe m’Cizungu na Cipwitikizi. Kutsogolo adzayamba kupezekanso m’vitundu vina.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani