LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w23 January tsa. 32
  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu:

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu:
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Kulitsani Ciyamikilo Canu pa Gulu la Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
w23 January tsa. 32

Mfundo Yothandiza Pa Kuŵelenga Kwanu:

Kodi mumakonda kuŵelenga nkhani zakuti “Mbili Yanga”?

M’maŵa uliwonse, m’bale wina na mkazi wake amaŵelenga nkhani imodzi, pa nkhani zakuti “Mbili Yanga.” Iwo anati: “Nkhani zimenezi zimatibweletsela cimwemwe komanso zimatilimbikitsa kwambili. Zimatikumbutsa kuti nafenso tingakhalebe okhulupilika pa mkhalidwe uliwonse umene tingakumane nawo.” Mlongo wina analemba kuti: “Nkhanizi n’zotonthoza, zolimbikitsa, komanso n’zogwila mtima. Abale na alongo athu amenewo amakhala na umoyo waphindu komanso watanthauzo. Nkhani zawo zimanilimbikitsa kucita zambili mu utumiki, komanso zimanithandiza kulimbikitsa ana anga kutumikila Yehova mwa kucita utumiki wa nthawi zonse.”

Nkhani zakuti “Mbili Yanga” zingakulimbikitseni kudziikila zolinga zabwino m’gulu la Mulungu, kugonjetsa zifooko, komanso kupilila mayeso aakulu mwacimwemwe. Kodi nkhani zimenezi mungazipeze kuti?

  • Pitani pa jw.org na kufufuza nkhani zakuti “Mbili Yanga.”

  • Kapena mungazifufuze pa LAIBULALE YA PA INTANETI™ ya Watchtower.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani