LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 154
  • “Cikondi Sicitha”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Cikondi Sicitha”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2019
  • Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 154

NYIMBO 154

“Cikondi Sicitha”

Yopulinta

(1 Akorinto 13:8)

  1. 1. Pakati pathu;

    Tiona cikondi—

    Cimene m’dziko mulibe.

    Timaonetsa

    Cikondi coona,

    Sitili mbali ya dziko.

    (MWANA WA KOLASI)

    M’lungu analonjeza.

    Cikondi sicitha.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu—

    Iye ni cikondi.

    Atikonda.

    Cikondi ici—

    Tizionetsana.

    Mu umoyo wathu,

    Tizikondanabe—

    Kwa muyaya.

  2. 2. Nthawi zambili

    Nkhawa na mavuto

    Zingatitsilize mphamvu,

    Kuthandizana

    Kumasangalatsa,

    M’lungu amatitonthoza.

    (MWANA WA KOLASI)

    Cikondi sicisila.

    Cipilila zonse.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu—

    Iye ni cikondi.

    Atikonda.

    Cikondi ici—

    Tizionetsana.

    Mu umoyo wathu,

    Tizikondanabe.

    (KOLASI)

    Yehova M’lungu—

    Iye ni cikondi.

    Atikonda.

    Cikondi ici—

    Tizionetsana.

    Mu umoyo wathu,

    Tizikondanabe—

    Kwa muyaya,

    Kwa muyaya,

    Kwa muyaya.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani