LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CA-copgm23 tsa. 4
  • Pezani Mayankha pa Mafunso Awa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pezani Mayankha pa Mafunso Awa
  • 2022-2023 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
  • Nkhani Zofanana
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2022-2023 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2019-2020 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woimila Nthambi
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2019-2020 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
  • Pezani Mayankho pa Mafunso Aya
    2020-2021 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
Onaninso Zina
2022-2023 Pulogilamu ya Msonkhano wa Dela—Wa Woyang’anila Dela
CA-copgm23 tsa. 4

Pezani Mayankho pa Mafunso Awa

  1. 1. Kodi tingaonetse bwanji kuti timayamikiladi malo athu m’banja la Yehova? (Aef. 4:3)

  2. 2. Kodi tingapangitse bwanji ena kumva kuti ni olandilidwa? Nanga n’cifukwa ciyani tiyenela kucita zimenezo? (Aroma 15:7)

  3. 3. Kodi tingathandize bwanji anthu ambili mmene tingathele kuti abwele m’banja la Yehova? (Aef. 2:17; 6:15)

  4. 4. Kodi tingalimbikitse bwanji mtendele? (Aef. 4:29; 5:1, 2; 6:13)

  5. 5. Kodi tingakulitse bwanji cikondi pa banja lathu lauzimu? (Aef. 1:15, 16)

© 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

CA-copgm23-CIN

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani