LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 4/1 tsa. 3
  • N’cifukwa Ciani Anthu Amapemphela?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • N’cifukwa Ciani Anthu Amapemphela?
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Nkhani Zofanana
  • Muyandikileni Mulungu Kupitila m’Pemphelo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Mwayi Wa Pemphelo
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • N’cifukwa Ciani Anthu Amapemphela?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tiziyamikila Mwayi Wathu wa Pemphelo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Onaninso Zina
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 4/1 tsa. 3

NKHANI YA PACIKUTO | N’CIFUKWA CIANI TIYENELA KUPEMPHELA?

N’cifukwa Ciani Anthu Amapemphela?

Kodi inu mumapemphela nthawi zonse? Anthu ambili amatelo, ngakhale amene sakhulupilila Mulungu. Nanga n’cifukwa ciani anthu amapemphela? Malinga ndi kauniuni wa ku France, hafu ya anthu kumeneko anakamba kuti amapemphela kapena kusinkhasinkha kuti “amveko bwino.” Mofanana ndi anthu a ku Europe, anthu a ku France samapemphela kuti alambile Mulungu. M’malo mwake, “amapemphela kuti atonthozedwe basi.” Kumbali ina, anthu ena amapemphela kwa Mulungu kokha akakumana ndi mavuto, ndipo amayembekezela kuti pempho lao liyankhidwe pamenepo.—Yesaya 26:16.

Nanga bwanji inuyo? Kodi mumaona pemphelo kukhala cabe njila yokuthandizani kukhala ndi maganizo oyenela? Ngati mumakhulupilila Mulungu, kodi mumaona kuti pemphelo limakuthandizani paumoyo wanu? Kapena mumaona kuti mapemphelo anu samayankhidwa? Baibulo lingakuthandizeni kupemphela kuti mukhale paubwenzi wabwino ndi Mulungu, osati kupemphela pofuna kutonthozedwa cabe.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani