LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 6/1 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 6/1 masa. 1-2

Zamkati

June 1, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

NKHANI ZOPHUNZILA

AUGUST 4-10, 2014

“Uzikonda Yehova Mulungu Wako”

TSAMBA 7 • NYIMBO: 3, 65

AUGUST 11-17, 2014

“Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondela Wekha”

TSAMBA 12 • NYIMBO: 84, 72

AUGUST 18-24, 2014

Kodi Mumaona Zofooka za Anthu Mmene Yehova Amazionela?

TSAMBA 17 • NYIMBO: 77, 79

AUGUST 25-31, 2014

Thandizani Ena Kupita Patsogolo

TSAMBA 22 • NYIMBO: 42, 124

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”

▪ “Uzikonda Mnzako Mmene Umadzikondela Wekha”

Nkhani ziŵili izi zifotokoza malamulo aakulu aŵili a m’Cilamulo amene Yesu anachula. Tidzaphunzila zimene Yesu anatanthauza pamene anakamba kuti tiyenela kukonda Yehova ndi mtima wathu wonse, moyo wathu wonse, ndi maganizo athu onse. Onani zimene tingacite kuti tionetse kuti timakonda anzathu mmene timadzikondela.

▪ Kodi Mumaona Zofooka za Anthu Mmene Yehova Amazionela?

▪ Thandizani Ena Kupita Patsogolo

Tingawathandize motani anthu amene amadziona kuti ndi ofooka? Iyi ndi mbali ina imene tidzakambitsilana m’nkhani zimenezi. Ndiponso, nkhanizi zidzaonetsa mmene tingathandizile abale acinyamata kapena obatizika catsopano kupita patsogolo..

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

Vuto la Padziko Lonse 3

Kodi Mulungu Amakuona Bwanji Kukoka Fodya? 4

Kodi Munadyapo Mkate wa Moyo? 27

Pali Ciyembekezo Cotani Ponena za Makolo Anga Akale? 30

Kuyankha Mafunso a m’Baibulo 32

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani