LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w14 11/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
w14 11/15 masa. 1-2

Zamkati

November 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

DECEMBER 29, 2014–JANUARY 4, 2015

Kodi Kuukitsidwa kwa Yesu Kumatanthauza Ciani kwa Ife?

TSAMBA 3 • NYIMBO: 5, 60

JANUARY 5-11, 2015

Cifukwa Cake Tifunika Kukhala Oyela

TSAMBA 8 • NYIMBO: 119, 17

JANUARY 12-18, 2015

Tifunika Kukhala Oyela m’Makhalidwe Athu Onse

TSAMBA 13 • NYIMBO: 65, 106

JANUARY 19-25, 2015

“Anthu Amene Mulungu Wao Ndi Yehova”

TSAMBA 18 • NYIMBO: 46, 63

JANUARY 26, 2015–FEBRUARY 1, 2015

‘Tsopano Ndinu Anthu a Mulungu’

TSAMBA 23 • NYIMBO: 112, 101

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Kodi Kuukitsidwa kwa Yesu Kumatanthauza Ciani kwa Ife?

M’nkhani ino, tidzaphunzila cifukwa cake timakhulupilila kuti Yesu anaukitsidwa ndipo ali moyo. Tidzaphunzilanso mmene kuukitsidwa kwa Kristu ku moyo wosafa wakumwamba kumatikhudzila, ndi mmene kumakhudzila nchito yathu monga alengezi a Ufumu.

▪ Cifukwa Cake Tifunika Kukhala Oyela

▪ Tifunika Kukhala Oyela m’Makhalidwe Athu Onse

Nkhani ziŵilizi, zimene ndi zozikidwa m’buku la Levitiko, zidzafotokoza cifukwa cake Yehova amafuna kuti anthu ake akhale oyela, ndi mmene tingaonetsele khalidwe limeneli. Tidzaphunzilanso mmene tingaonetsele kuti ndife oyela m’makhalidwe athu onse.

▪ “Anthu Amene Mulungu Wao Ndi Yehova”

▪ ‘Tsopano Ndinu Anthu a Mulungu’

Anthu ena amene timaphunzila nao Baibulo, samakhulupilila kuti Yehova ali ndi gulu limodzi cabe padziko lapansi. Iwo amaganiza kuti kungokhala munthu wabwino n’kokwanila kuti ukondweletse Mulungu, mosasamala kanthu za cipembedzo cako. Nkhani ziŵilizi, zidzatithandiza kuzindikila anthu a Mulungu, ndi kugwilizana nao potumikila Yehova.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

28 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

31 Za m’Nkhokwe Yathu

PACIKUTO: Ofalitsa a Ufumu alalikila ku Santiago de Cuba, mzinda wina waukulu wa pa cilumba umene ndi wochuka cifukwa ca nyimbo za kumaloko ndi magule ake

KU CUBA

KULI ANTHU

11,163,934

OFALITSA

96,206

APAINIYA ANTHAWI ZONSE

9,040

270 ofalitsa ogontha amagwilitsila nchito cinenelo camanja ca ku Cuba
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani