LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 2/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 2/15 masa. 1-2

Zamkati

February 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

APRIL 6-12, 2015

Khalani Wodzicepetsa ndi Wacifundo Monga Yesu

TSAMBA 5 • NYIMBO: 5, 84

APRIL 13-19, 2015

Khalani Wolimba Mtima ndi Wozindikila Monga Yesu

TSAMBA 10 • NYIMBO: 99, 108

APRIL 20-26, 2015

Kukonzekeletsa Anthu ‘Kuphunzila Zokhudza Yehova’

TSAMBA 19 • NYIMBO: 98, 104

APRIL 27, 2015–MAY 3, 2015

Yehova Akutsogolela Nchito Yathu Yophunzitsa Padziko Lonse

TSAMBA 24 • NYIMBO: 103, 66

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Khalani Wodzicepetsa ndi Wacifundo Monga Yesu

▪ Khalani Wolimba Mtima ndi Wozindikila Monga Yesu

Baibulo limatilimbikitsa kutsatila mapazi a Yesu mosamala kwambili. (1 Pet. 2: 21) Popeza ndife opanda ungwilo, kodi n’zotheka kutsatila citsanzo cangwilo ca Yesu? Nkhani yoyamba pa nkhani ziŵili izi idzafotokoza mmene tingakhalile odzicepetsa ndi acifundo monga Yesu. Nkhani yaciŵili idzaonetsa mmene tingatengele citsanzo cake pankhani yokhala wolimba mtima ndi wozindikila.

▪ Kukonzekeletsa Anthu ‘Kuphunzila Zokhudza Yehova’

▪ Yehova Akutsogolela Nchito Yathu Yophunzitsa Padziko Lonse

Nkhani yoyamba pa nkhani ziŵili izi idzafotokoza mmene Yehova anathandizila ophunzila a Yesu m’nthawi ya atumwi kulalikila uthenga wabwino. M’nkhani yotsatila, tidzakambilana zinthu zina zamakono zimene zatithandiza kufalitsa uthenga wa Ufumu kwa anthu a mitima yabwino padziko lonse lapansi.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Mphatso Yosangalatsa ya Anthu a ku Japan

15 Pitilizani Kukhala Wacangu mu Utumiki

29 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

31 Za m’Nkhokwe Yathu

PA CIKUTO: Akugaŵila magazini a Galamukani! mu ulaliki wa kunyumba ndi nyumba pacilumba ca Bali, ndipo alandilidwa mogwilizana ndi cikhalidwe ca ku Indonesia

KU INDONESIA

KULI ANTHU

237,600,000

OFALITSA

24,521

APAINIYA A NTHAWI ZONSE

2,472

Kuli apainiya apadela 369 amene akutumikila pa zilumba zosiyanasiya zokwana 28

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani