LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 3/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 3/15 masa. 1-2

Zamkati

March 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

MAY 4-10, 2015

“Munavomeleza Kuti Zimenezi Zicitike”

TSAMBA 7 • NYIMBO: 65, 64

MAY 11-17, 2015

Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?

TSAMBA 12 • NYIMBO: 108, 24

MAY 18-24, 2015

Zimene Tiphunzilapo pa Fanizo la Matalente

TSAMBA 19 • NYIMBO: 101, 116

MAY 25-31, 2015

Kuthandiza Abale a Kristu Mokhulupilika

TSAMBA 25 • NYIMBO: 107, 63

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ “Munavomeleza Kuti Zimenezi Zicitike”

▪ Kodi ‘Mudzakhalabe Maso’?

M’nkhani yoyamba, tidzakambilana mmene Yehova wakhala akutsogolela anthu ake kuphunzila zinthu pang’onopang’ono m’njila yosavuta ndi yomveka bwino. M’nkhani yaciŵili, tidzakambilana fanizo la Yesu la anamwali 10 ndi kuona mmene lingatithandizile kukhala maso mwakuuzimu masiku ano.

▪ Zimene Tiphunzilapo pa Fanizo la Matalente

▪ Kuthandiza Abale a Kristu Mokhulupilika

Pofotokoza cizindikilo ca kukhalapo kwake, Yesu anakamba mafanizo aŵili amene tidzakambilana. Fanizo loyamba ndi lokhudza akapolo amene anapatsidwa matalente, ndipo lina ndi lokhudza mmene anthu adzalekanitsidwila monga nkhosa ndi mbuzi. Tidzaphunzila cifukwa cake Yesu anafotokoza mafanizo amenewa ndi mmene amatikhudzila.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Tinapeza Nchito Yopindulitsa Kwambili

17 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

30 Kodi Kukwatiwa “Mwa Ambuye”—N’kofunikabe?

PACIKUTO: Anthu ambili amapita ku Copán kukaona mabwinja ocititsa cidwi, koma Mboni za Yehova kumeneko zimathandiza anthu kuyembekezela zinthu zabwino mtsogolo

KU HONDURAS

KULI ANTHU

8,111,000

OFALITSA

22,098

APAINIYA ANTHAWI ZONSE

3,471

Cinenelo cacikulu ku Honduras ndi Cisipanishi. Koma ofalitsa 365 m’mipingo 12 amagwilitsila nchito cinenelo cochedwa Garifuna. Kulinso mipingo 11 komanso magulu atatu amene amagwilitsila nchito cinenelo camanja ca ku Honduras

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani