LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 5/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 5/15 masa. 1-2

Zamkati

May 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

JUNE 29, 2015–JULY 5, 2015

Khalani Maso! Satana Akufuna Kukumezani

TSAMBA 9 • NYIMBO: 54, 43

JULY 6-12, 2015

Mungapambane Polimbana Ndi Satana

TSAMBA 14 • NYIMBO: 60, 100

JULY 13-19, 2015

‘Anaona’ Malonjezo a Mulungu

TSAMBA 19 • NYIMBO: 81, 134

JULY 20-26, 2015

Muzitsanzila Mulungu Amene Watilonjeza Moyo Wosatha

TSAMBA 24 • NYIMBO: 12, 69

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Khalani Maso! Satana Akufuna Kukumezani

▪ Mungapambane Polimbana Ndi Satana

Baibulo limayelekezela Satana ndi mkango wobangula umene ukuŵendelela nyama. Iye ndi wamphamvu, wankhanza, ndi wacinyengo. Nkhani ziŵilizi zidzatithandiza kuona cifukwa cake tifunika kulimbana ndi mdani wathu wamkulu ameneyu. Zidzatithandizanso kudziŵa mmene tingadzitetezele ku njila zake zacinyengo.

▪ ‘Anaona’ Malonjezo a Mulungu

▪ Muzitsanzila Mulungu Amene Watilonjeza Moyo Wosatha

Mphamvu imene tili nayo yotha kuganizila zinthu zimene sitinazionepo tingaigwilitsile nchito mwanzelu kapena molakwika. M’nkhani ziŵilizi, tidzakambilana zitsanzo za m’Baibulo zimene zingatithandize pankhaniyi. Tidzaphunzila mmene mphamvu yotha kuganizila zinthu zimene sitinazionepo ingatithandizile kukhala ndi cikhulupililo colimba, ndi kutsanzila makhalidwe a Yehova monga cikondi, kukoma mtima, nzelu, ndi cimwemwe.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 Kukumbukila Cikondi Canga ca Poyamba Kwandithandiza Kupilila

29 Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi

31 Za m’Nkhokwe Yathu

PACIKUTO: Abale aŵili akucititsa phunzilo la Baibulo

KU ARMENIA

KULI ANTHU

3,026,900

OFALITSA

11,143

APAINIYA ANTHAWI ZONSE:

2,205
23,844

Anthu amene anapezeka pa Cikumbutso ku Armenia pa April 14, 2014 anali oculuka kuwilikiza kaŵili poyelekezela ndi ciŵelengelo ca ofalitsa a m’dzikolo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani