LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 8/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 8/15 masa. 1-2

Zamkati

August 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

NKHANI ZOPHUNZILA

SEPTEMBER 28, 2015–OCTOBER 4, 2015

Muzisinkhasinkha za Cikondi Cosatha ca Yehova

TSAMBA 9

OCTOBER 5-11, 2015

Yembekezelanibe!

TSAMBA 14

OCTOBER 12-18, 2015

Konzekelani Kudzakhala m’Dziko Latsopano

TSAMBA 19

OCTOBER 19-25, 2015

Samalani ndi Anthu Ogwilizana Nao Masiku Ano Otsiliza

TSAMBA 24

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Muzisinkhasinkha za Cikondi Cosatha ca Yehova

Cikondi cimene Yehova amaonetsa anthu ake n’cosatha. Nkhaniyi ifotokoza mmene Yehova waonetsela cikondi cake. Kusinkhasinkha mmene Yehova wationetsela cikondi kudzatithandiza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi iye.

▪ Yembekezelanibe!

▪ Konzekelani Kudzakhala m’Dziko Latsopano

Ngakhale kuti papita nthawi yaitali, tiyenela kukhalabe ndi ciyembekezo cakuti madalitso a Ufumu adzakwanilitsidwa. Tili ndi zifukwa zomveka zoyembekezela malonjezo a m’Baibulo. Nkhanizi zifotokoza mmene tingacitile zimenezi.

▪ Samalani ndi Anthu Ogwilizana Nao Masiku Ano Otsiliza

N’cifukwa ciani m’pofunika kusamala ndi anthu ogwilizana nao masiku ano otsiliza? Kodi Mau a Mulungu amatithandiza bwanji kucita zimenezi? Mafunso amenewa ndi ena adzayankhidwa m’nkhani ino.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

3 “Zilumba Zambili Zisangalale”

29 Kodi Tiphunzilapo Ciani pa Zimene Jowana Anacita?

31 Za m’Nkhokwe Yathu

PACIKUTO: M’bale wacinyamata akucita ulaliki wamwai ndipo akuonetsa munthu wina vidiyo pa jw.org mu mzinda wa Esperanza

ARGENTINA

KULI ANTHU

42,670,000

OFALITSA

150,171

APAINIYA ANTHAWI ZONSE

18,538

MAPHUNZILO A BAIBULO

126,661

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2014)

307,654

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani