LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 August tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 August tsa. 2

Zamkati

3 Napeza Cimwemwe Cifukwa Copatsa

MLUNGU WA SEPTEMBER 26–OCTOBER 2, 2016

8 Cikwati—Ciyambi na Cifuno Cake

MLUNGU WA OCTOBER 3-9, 2016

13 Kupangitsa Cikwati Cacikhiristu Kukhala Cacimwemwe

M’nkhani yoyamba tidzakambilana za ciyambi ca cikwati, mmene Cilamulo ca Mose cinatsogolela cikwati, ndi mfundo imene Yesu anakhazikitsa yokhuza cikwati. M’nkhani yaciŵili, tidzaona mmene Malemba amaunikila bwino udindo wa mwamuna ndi wa mkazi m’banja.

18 Fufuzani Cinthu Camtengo Wapatali Kuposa Golide

MLUNGU WA OCTOBER 10-16, 2016

20 Kodi Mumaona Kufunika Kopita Patsogolo Kuuzimu?

MLUNGU WA OCTOBER 17-23

25 Kodi Mumaona Kufunika Kophunzitsa Ena?

Ndife okondwela kuti nchito yolalikila za Ufumu yapita patsogolo kwambili. Koma kodi timaona kuti umenewu ni mwayi woonjezela utumiki wathu kwa Mulungu? Tingacite ciani kuti tipite patsogolo panthawi imodzi-modzi tithandizenso ophunzila Baibulo kupita patsogolo? N’cifukwa ciani pafunika kuti ena aphunzitsidwe? Nkhani ziŵilizi ziyankha mafunso ofunika amenewa.

30 Mafunso Ocokela Kwa Aŵelengi

31 Za M’nkhokwe Yathu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani