LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 September tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 September tsa. 2

Zamkati

MLUNGU WA OCTOBER 24-30, 2016

3 “Manja Anu Asakhale Olefuka”

MLUNGU WA OCTOBER 31, 2016–NOVEMBER 6, 2016

8 Cilimikani pa Kulimbana Kuti Mupeze Madalitso a Yehova

Mavuto na nkhawa za mu umoyo zingatipanikize ndi kucititsa manja athu ophiphilitsa kulefuka. Nkhani ziŵilizi zidzaonetsa mmene Yehova amatithandizila ndi dzanja lake lamphamvu kuti tipilile mavuto. Tidzaonanso mmene tingapitilizile kucilimika pa “kulimbana” kuti tipeze madalitso a Yehova.

13 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

14 Kuteteza Uthenga Wabwino Pamaso pa Akulu-akulu a Boma

MLUNGU WA NOVEMBER 7-13, 2016

17 Kodi Mavalidwe Anu Amalemekeza Mulungu?

Atumiki a Mulungu padziko lonse amafuna kuvala na kudzikonza moyenelela. Amavala zovala zooneka bwino, zoyela, ndi zololeka kudela la kwawo, komanso zogwilizana ndi mfundo za m’Malemba. Nanga mungacite ciani kuti mavalidwe anu azilemekeza Mulungu?

22 Ubwino Wotsatila Malangizo a Yehova

MLUNGU WA NOVEMBER 14-20, 2016

23 Wacicepele, Limbitsa Cikhulupililo Cako

MLUNGU WA NOVEMBER 21-27, 2016

28 Makolo, Thandizani Ana Anu Kukhala na Cikhulupililo

M’nkhani ziŵilizi, tidzaona mmene acicepele angaseŵenzetsele luso lawo la kulingalila kuti alimbitse cikhulupililo cawo na kuciteteza. Tidzaonanso mmene makolo acikhiristu angapezele njila zokondweletsa zothandizila ana awo kukulitsa cikhulupililo mwa Mulungu ndi Mau ake.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani