LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 November tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 November tsa. 2

Zamkati

3 Mau Amene Anali Atanthauzo Kwambili

MLUNGU WA DECEMBER 26, 2016–JANUARY 1, 2017

4 ‘Pitilizani Kulimbikitsana Tsiku na Tsiku’

Yehova Mulungu na Yesu Khiristu ni zitsanzo zabwino ngako pankhani yolimbikitsa ena. Nayenso mtumwi Paulo anaona kuti kulimbikitsa ena n’kofunika ngako. Kutengela citsanzo cawo kudzatithandiza kumakonda anthu ena na kuwalimbikitsa pa nyumba yathu na ku Nyumba ya Ufumu.

MLUNGU WA JANUARY 2-8, 2017

9 Gulu Lake Ladongosolo Monga mwa Buku la Mau Ake

MLUNGU WA JANUARY 9-15, 2017

14 Kodi Mumalemekeza Buku Lake la Yehova?

Nkhani izi zidzayankha mafunso aya: N’cifukwa ciani olambila Yehova ayenela kucita zinthu mwadongosolo? Tingakhale bwanji adongosolo molingana na Buku la Mau a Mulungu? Nanga tingaonetse bwanji kuti timacilikiza mokhulupilika gulu la Yehova?

19 “Nchitoyi Ndi Yaikulu”

MLUNGU WA JANUARY 16-22, 2017

21 Kuitaniwa Kucoka mu Mdima

MLUNGU WA JANUARY 23-29, 2017

26 Anamasuka Kucoka ku Cipembedzo Conama

Nkhanizi zidzafotokoza nthawi imene anthu a Mulungu analoŵa mu ukapolo wa m’Babulo Wamkulu, ndi khama limene Akhiristu odzozedwa anaonetsa cakumapeto kwa ma 1800 kuti amvetse Mau a Yehova molongosoka. Tidzaphunzilanso za kaimidwe kolimba kamene Ophunzila Baibo anatenga kulinga kwa Babulo Wamkulu. Tidzaonanso kuti n’liti pamene Akhiristu anamasuka mu ukapolo kwa Babulo Wamkulu.

31 Za M’nkhokwe Yathu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani