LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 November masa. 1-2
  • Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 November masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila ya November 2016

Yophunzila

NOVEMBER 2016

NKHANI ZOPHUNZILA M’MLUNGU WA: DECEMBER 26, 2016–JANUARY 29, 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

KU ANGOLA

Mu mzinda wa Benguela, apainiya apadela atsogoza phunzilo la Baibo m’cinenelo ca manja, mwa kuseŵenzetsa kabulosha ka Mvetselani kwa Mulungu Kuti Mukhale ndi Moyo Wamuyaya. Ofalitsa 10 osamva mu mzindawo anakondwela ngako kuti anthu 62 anapezeka pa Cikumbutso mu 2015

OFALITSA

115,948

MAPHUNZILO A BAIBO

502,848

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2015)

529,827

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi ni zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani