LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 January masa. 1-2
  • Magazini Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Magazini Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 January masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila, January 2017

Magazini Yophunzila

JANUARY 2017

NKHANI ZOPHUNZILA: FEBRUARY 27–APRIL 2, 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

CHILE

Ofalitsa a kum’mwela kwa dziko la Chile akuyenda m’mbali mwa mtsinje wodutsa m’nkhalango na m’mapili a Andes okhala ndi sinowu (snow) pamwamba pake. Ali pa nchito yapadela yokalalikila kwa anthu akutali pamene nyengo yakhalako bwino.

OFALITSA

76,296

MAPHUNZILO A BAIBO

64,178

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2015)

174,761

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi ni zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani