LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 February tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 February tsa. 2

Zamkati

WIKI YA APRIL 3-9, 2017

3 Colinga ca Yehova Cidzakwanilitsika

WIKI YA APRIL 10-16, 2017

8 Dipo—‘Mphatso Yangwilo’ Yocokela kwa Atate

Nsembe ya dipo ya Khiristu ni yofunika kwambili pa cikhulupililo cathu, komanso pa colinga ca Yehova ca poyamba cokhudza mtundu wa anthu. Nkhani ziŵilizi, zidzafotokoza cifukwa cake panafunikila dipo, zimene dipolo linakwanilitsa, ndi mmene tingaonetsele kuti timayamikila na mtima wonse mphatso imeneyi yoposa zonse yocokela kwa Atate wathu wakumwamba.

13 Mbili Yanga​—Tinaona Cisomo ca Mulungu m’Njila Zambili

WIKI YA APRIL 17-23, 2017

18 Yehova Amatsogolela Anthu Ake

WIKI YA APRIL 24-30, 2017

23 N’ndani Akutsogolela Anthu a Mulungu Masiku Ano?

Kwa zaka zambili, Yehova wakhala akusankha amuna kuti atsogolele. N’cifukwa ciani tingakambe kuti Yehova wakhala akuthandiza amuna amenewo? Nanga tidziŵa bwanji kuti akuthandiza kapolo wokhulupilika ndi wanzelu masiku ano? M’nkhanizi, tidzaphunzila maumboni atatu amene akhala akudziŵikitsa anthu oimilako Mulungu.

29 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

31 Za M’nkhokwe Yathu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani