LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 March masa. 1-2
  • Magazini Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Magazini Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 March masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila, March 2017

Magazini Yophunzila

MARCH 2017

NKHANI ZOPHUNZILA: MAY 1-​28, 2017

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

ROMANIAMkulu ameneyu ndi mkazi wake amaona kuti nthawi yabwino yolalikila kwa anthu onga nkhosa kumpoto kwa Romania, ndi pa Sondo, pambuyo pa misonkhano. Anthu amenewa aphatikizapo azimayi aŵili amene akukonza ubweya wa nkhosa.

OFALITSA

40,575

MAPHUNZILO A BAIBO

25,623

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2015)

78,300

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi ni zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani