LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 July tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 July tsa. 2

Zamkati

3 Anadzipeleka na Mtima Wonse—Ku Turkey

WIKI YA AUGUST 28, 2017–SEPTEMBER 3, 2017

7 Kufunafuna Cuma Ceni-ceni

Nkhani iyi idzafotokoza mmene tingaseŵenzetsele cuma cathu kuti ‘tidzipezele mabwenzi’ kumwamba. (Luka 16:9) Idzafotokozanso mmene tingapewele kukhala akapolo kwa anthu amalonda m’dzikoli, komanso zimene tingacite kuti titumikile Yehova mokwanila.

WIKI YA SEPTEMBER 4-10, 2017

12 “Lilani Ndi Anthu Amene Akulila”

Kodi Mkhristu angapilile bwanji imfa ya munthu amene anali kum’konda? Yehova amapeleka citonthozo ca panthawi yake kupitila mwa Yesu Khristu, Malemba, ndi mpingo wacikhristu. Nkhaniyi idzafotokoza mmene ise tingapezele citonthozo, ndiponso mmene tingatonthozele ena amene afedwa.

WIKI YA SEPTEMBER 11-17, 2017

17 N’cifukwa Ciani Tifunika Kutamanda Yehova?

Salimo 147 imalimbikitsa anthu a Mulungu mobweleza-bweleza kuti afunika kutamanda Yehova. N’zinthu ziti zokhudza Yehova zimene zinapangitsa wolemba salimoyi kuona kuti Mulungu ni wofunika kutamandidwa? Nkhani iyi idzafotokoza zinthu zimenezo. Idzafotokozanso cifukwa cake na ise tifunika kukhala ofunitsitsa kutamanda Mulungu wathu.

WIKI YA SEPTEMBER 18-24, 2017

22 Mulungu “Akwanilitse Zofuna Zanu”

Abale na alongo ambili acicepele ayamba utumiki wa nthawi zonse. Kodi n’zimenenso imwe mufuna? Nkhani iyi ipeleka malangizo abwino ocokela m’Malemba, amene adzakuthandizani kukhala na zolinga zabwino zimene zingakuthandizeni kuti mtsogolo, mudzakhale na umoyo wabwino ndi wacimwemwe.

27 Mungapambane Bwanji Nkhondo Yoteteza Maganizo Anu?

31 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani