LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 August tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 August tsa. 2

Zamkati

WIKI YA SEPTEMBER 25, 2017–OCTOBER 1, 2017

3 Kodi Mudzayembekezela Moleza Mtima?

WIKI YA OCTOBER 2-8, 2017

8 “Mtendele wa Mulungu . . . Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse”

Nkhani yoyamba idzafotokoza cifukwa cake tifunika kuyembekezela Yehova. Tidzakambilananso zimene tingaphunzile kwa amuna ndi akazi okhulupilika akale pankhani yombekezela Mulungu moleza mtima. Nkhani yaciŵili idzaonetsa mmene Yehova nthawi zina amacitila zinthu m’njila imene sitinali kuyembekezela. Kukambilana zimenezi kudzalimbitsa cikhulupililo cathu mwa iye pamene tiyembekezela moleza mtima kuti atithandize pa mavuto athu.

13 Mbili Yanga Kupilila Ziyeso Kumabweletsa Madalitso

WIKI YA OCTOBER 9-15, 2017

17 Mmene Timavulila Umunthu Wakale ndi Kusauvalanso

WIKI YA OCTOBER 16-22, 2017

22 Mmene Timavalila Umunthu Watsopano ndi Kusauvulanso

Nkhani yoyamba idzafotokoza zimene kuvula umunthu wakale kumatanthauza na cifukwa cake tifunika kucita zimenezi mwamsanga. Idzafotokozanso zimene tingacite kuti tipewe kubwelelanso ku umunthu wakale. Nkhani yaciŵili idzafotokoza makhalidwe angapo amene ali mbali ya umunthu watsopano. Idzafotokozanso mmene tingaonetsele makhalidwe amenewa mu umoyo wathu wa tsiku na tsiku ndi muulaliki.

27 Cikondi—Khalidwe Lamtengo Wapatali

30 Za M’nkhokwe Yathu

32 Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani