Yophunzila
NOVEMBER 2017
NKHANI ZOPHUNZILA: DECEMBER 25, 2017–JANUARY 28, 2018
© 2017 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
PIKICA YA PACIKUTO:
NICARAGUA
Alongo aŵili akulalikila uthenga wa m’Baibo kwa munthu wamalonda m’tauni ya Tipitapa
OFALITSA
28,642
MAPHUNZILO A BAIBO
42,298
OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2016)
88,308
Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi n’zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.
Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.
Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.