LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 December masa. 1-2
  • Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 December masa. 1-2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila, December 2017

Yophunzila

DECEMBER 2017

NKHANI ZOPHUNZILA: JANUARY 29–FEBRUARY 25, 2018

© 2017 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

CÔTE D’IVOIRE

Dziko la Côte d’Ivoire (limene kale linali kuchedwa Ivory Coast) ndiye kumene amalima kwambili nyemba za koko, zimene amapangila cokoleti. Nyembazi amaziyanika pa dzuwa kuti ziume. Mpainiya akulalikila uthenga wofunika kwambili wa m’kabuku kakuti Uthenga Wabwino, kwa munthu amene akuyanika nyemba za koko

OFALITSA

11,133

MAPHUNZILO A BAIBO

28,274

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2016)

76,526

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi n’zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani