LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 December tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 December tsa. 2

Zamkati

WIKI YA JANUARY 29, 2018–FEBRUARY 4, 2018

3 “Ndidziŵa Kuti Adzauka”

WIKI YA FEBRUARY 5-11, 2018

8 “Ine Ndili Ndi Ciyembekezo mwa Mulungu”

Ni zocitika zakale ziti zimene zinathandiza Akhristu kukhala na cikhulupililo cakuti akufa adzauka? Nanga kuganizila zocitika zimenezo komanso ciyembekezo cimene anthu ena okhulupilika akale anali naco, kuyenela kukhudza bwanji ciyembekezo canu? Nkhani zimenezi zidzalimbitsa cikhulupililo canu cakuti akufa adzauka.

13 Kodi Mukumbukila?

14 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga

16 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga

WIKI YA FEBRUARY 12-18, 2018

18 Makolo—Thandizani Ana Anu Kupeza ‘Nzelu Zowathandiza Kuti Akapulumuke’

WIKI YA FEBRUARY 19-25, 2018

23 Acicepele—“Pitilizani Kukonza Cipulumutso Canu”

Anthu masauzande ambili amabatizika caka ciliconse. Ena mwa anthu amenewa ni acicepele. Kubatizika kumatsegula mwayi wolandila madalitso ambili, koma kumabweletsanso udindo. Makolo, kodi mungawathandize bwanji ana anu kukonzekela ubatizo? Ngati ndinu wacicepele wobatizika kapena amene mufuna kudzabatizika, kodi mungalimbitse bwanji ubwenzi wanu na Yehova?

28 Mbili Yanga​—N’nasiya Zinthu Zina Pofuna Kutsatila Ambuye

32 Mlongoza Nkhani wa Nsanja ya Mlonda 2017

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani