LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • wp18 na. 3 tsa. 2
  • Mau oyamba

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mau oyamba
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mulungu amamvela bwanji akaona kuti muvutika?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2018
wp18 na. 3 tsa. 2

Mau Oyamba

KODI MULUNGU AMAKUDELANI NKHAWA?

Masoka aakulu akacitika kapena pamene anthu avutika na kufa, tingadzifunse ngati Mulungu amaona komanso kukhudzidwa na zimenezi. Baibo imakamba kuti:

“Pakuti maso a Yehova ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzelo lawo, koma nkhope ya Yehova imakwiyila anthu ocita zoipa.”—1 Petulo 3:12.

Nsanja ya Mlonda ino, ionetsa mmene Mulungu amatithandizila komanso zimene akucita kuti acotsepo mavuto onse.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani