LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 April tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 April tsa. 2

Zamkati

WIKI YA JUNE 4-10, 2018

3 Njila Yopezela Ufulu Weni-weni

WIKI YA JUNE 11-17, 2018

8 Tumikilani Yehova, Mulungu wa Ufulu

Anthu pa dziko lonse amafunitsitsa kukhala na ufulu waukulu. Kodi Akhristu afunika kuuona bwanji ufulu? Nkhani ziŵilizi zidzafotokoza tanthauzo la ufulu weni-weni, mmene tingaupezele, na mmene tingaseŵenzetsele ufulu wokhala na malile umene tili nawo, kuti tipindule mu umoyo wathu na kupindulitsanso ena. Koposa zonse, tidzaphunzila mmene tingalemekezele Yehova Mulungu, Gwelo la ufulu weni-weni.

13 Amuna a Paudindo —Tengelani Citsanzo ca Timoteyo

WIKI YA JUNE 18-24, 2018

15 Tengelani Yehova —Mulungu Amene Amapeleka Cilimbikitso

WIKI YA JUNE 25, 2018–JULY 1, 2018

20 “Tiyeni Tilimbikitsane, Ndipo Tiwonjezele Kucita Zimenezi”

Nkhanizi zionetsa kuti nthawi zonse Yehova wakhala akulimbikitsa atumiki ake, ndiponso kuti kwa zaka zambili, atumiki akewo akhala akutengela citsanzo cake. Tidzaona cifukwa cake kulimbikitsana n’kofunika maningi masiku ano.

WIKI YA JULY 2-8, 2018

25 Acicepele, Kodi Mumaika Zolinga Zauzimu Patsogolo?

Acicepele mu mpingo wacikhristu amapindula ngati aika mtima wawo pa kucita zinthu zokondweletsa Yehova. Nkhaniyi idzafotokoza zifukwa zake acicepele afunika kuika patsogolo nchito yolalikila, komanso kudziikila zolinga zauzimu akali aang’ono.

30 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani