LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 June tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 June tsa. 2

Zamkati

WIKI YA AUGUST 6-12, 2018

3 “Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino”

WIKI YA AUGUST 13-19, 2018

8 Tikhale Amodzi, Monga Mmene Yehova na Yesu Alili Amodzi

Anthu m’nthawi ya Yesu anali ogaŵikana cifukwa cosiyana pa zandale, cikhalidwe, kapena mitundu. M’nkhani ziŵilizi, tidzaphunzila mmene Khristu anaphunzitsila otsatila ake kuti akhale ogwilizana na kupewa tsankho limene limagaŵanitsa anthu. Tidzaphunzilanso mmene tingatengele citsanzo cawo m’dziko logaŵikanali.

13 Akanayanjidwa na Mulungu

WIKI YA AUGUST 20-26, 2018

16 Lolani Malamulo a Mulungu na Mfundo Zake Kuphunzitsa Cikumbumtima Canu

Kuti cikumbumtima cathu cizititsogolela bwino, tifunika kuciphunzitsa. Mwacikondi, Yehova anatipatsa malamulo na mfundo zimene zingatithandize kuphunzitsa bwino cikumbumtima cathu na kuona zinthu mmene iye amazionela. Nkhaniyi idzafotokoza mmene tingaseŵenzetsele bwino mfundo za m’Baibo mu umoyo wathu.

WIKI YA AUGUST 27, 2018–SEPTEMBER 2, 2018

21 “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke

Yesu analimbikitsa ophunzila ake kuti ayenela kuonetsa kuwala kwawo kuti Mulungu alemekezeke. Nkhaniyi idzafotokoza malangizo abwino amene tikawaseŵenzetsa angatithandize kuonetsa kuwala kwathu mokwanila.

26 Mbili Yanga—N’natonthozedwa pa Mavuto Anga Onse

30 Mphamvu ya Moni

32 Kodi Mukumbukila?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani