LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 August tsa. 2
  • Yophunzila

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yophunzila
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
  • Tumitu
  • NKHANI ZOPHUNZILA: OCTOBER 1-28, 2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 August tsa. 2
Nsanja ya Mlonda Yophunzila, August 2018

Yophunzila

AUGUST 2018

NKHANI ZOPHUNZILA: OCTOBER 1-28, 2018

© 2018 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

PIKICA YA PACIKUTO:

MALAWI

Woyang’anila dela na mkazi wake akonzeka kuti ayambe ulendo wopita kukacezela mpingo wina. Pa njinga zawo anyamula mabuku ophunzilila Baibo, pulojekita, zokuzila mawu, na katundu wawo wina.

OFALITSA

93,412

MAPHUNZILO A BAIBO

145,504

OPEZEKA PA CIKUMBUTSO (2017)

315,784

Magazini ino si yogulitsa. Colinga cake ni kuthandiza pa nchito yophunzitsa Baibo imene ikucitika padziko lonse lapansi. Ndalama zoyendetsela nchitoyi n’zimene anthu amapeleka mwa kufuna kwawo.

Ngati mufuna kupeleka ndalama zothandizila nchitoyi, yendani pa www.jw.org.

Baibo imene taseŵenzetsa ni Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika, kusiyapo ngati taonetsa ina. Komabe, ena mwa masipeling’i a Cinyanja m’magazini ino tatsatila malamulo a m’buku lakuti A Unified Standard Orthography for South-Central African Languages.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani