LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 October tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 October tsa. 2

Zamkati

3 1918—Zimene Zinacitika Zaka 100 Zapitazo

WIKI YA DECEMBER 3-9, 2018

6 Tizikamba Zoona

WIKI YA DECEMBER 10-16, 2018

11 Kuphunzitsa Coonadi

Anthu ambili masiku ano amakonda kunama. Kodi bodza linayamba bwanji? Nanga ni bodza liti limene linabweletsa mavuto aakulu kwambili kwa anthu? Tingapewe bwanji kusoceletsedwa? Nanga tingaonetse bwanji kuti timakamba zoona kwa wina na mnzake? Tingaseŵenzetse bwanji Thuboksi yathu ya Zida Zophunzitsila pophunzitsa coonadi mu ulaliki? Nkhani ziŵilizi zidzayankha mafunso amenewa.

17 Mbili Yanga Yehova Anan’dalitsa Kwambili Cifukwa ca Zimene N’nasankha

WIKI YA DECEMBER 17-23, 2018

22 Tizidalila Mtsogoleli Wathu —Khristu

WIKI YA DECEMBER 24-30, 2018

27 Khalanibe na Mtendele wa mu Mtima Olo Pamene Zinthu Zasintha

Pokhala anthu opanda ungwilo, nthawi zambili timakhala na nkhawa kwambili ngati zinthu zasintha mu umoyo wathu kapena m’gulu la Mulungu. Nkhani ziŵilizi zidzatithandiza kukhalabe na mtendele wa mu mtima, komanso kudalila Mtsogoleli wathu, Khristu, pamene zinthu zasintha mosayembekezeleka mu umoyo wathu.

32 Kodi Mudziŵa?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani