LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 November tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 November tsa. 2

Zamkati

WIKI YA DECEMBER 31, 2018–JANUARY 6, 2019

3 “Gula Coonadi Ndipo Usacigulitse”

WIKI YA JANUARY 7-13, 2019

8 “Ndidzayenda M’coonadi Canu”

Nkhani ziwilizi zidzatilimbikitsa kuti tiziyamikila coonadi camtengo wapatali cimene Yehova watiphunzitsa. Coonadi cimeneci n’camtengo wapatali kuposa zinthu zilizonse zimene tinatailapo kuti ticipeze. Tidzakambilananso zimene tingacite kuti tipitilize kuona coonadi kukhala camtengo wapatali, komanso kuti tisacigulitse kapena kunyalanyaza mfundo zina za coonadi cimene Yehova watiphunzitsa.

WIKI YA JANUARY 14-20, 2019

13 Dalilani Yehova Kuti Mukhalebe na Moyo

Buku la Habakuku lionetsa zimene tingacite kuti tipitilize kudalila Yehova pamene tikumana na mavuto. Nkhani iyi idzatithandiza kuona kuti tikakhala na nkhawa kapena ngati tikukumana na mavuto kapena ziyeso, tifunika kudalila Mulungu. Tikatelo, iye adzatithandiza kupilila.

WIKI YA JANUARY 21-27, 2019

18 Kodi Mumayendela Maganizo a Ndani?

WIKI YA JANUARY 28, 2019–FEBRUARY 3, 2019

23 Kodi Mumayesetsa Kuona Zinthu Mmene Yehova Amazionela?

Pamene tikula mwauzimu, timayamba kuona kuti kaonedwe ka zinthu ka Yehova ndiko kabwino koposa. M’nkhani ziwilizi tidzakambilana zimene tingacite kuti tipewe kuyendela maganizo a dzikoli, na kuwongola maganizo athu kuti tiziona zinthu mmene Yehova amazionela.

28 Kukoma Mtima—Khalidwe Limene Limaonekela M’mawu na M’zocita

31 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga

32 Ni Mphatso Yanji Imene Tingam’patse Yehova?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani