LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 December tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 December tsa. 2

Zamkati

WIKI YA FEBRUARY 4-10, 2019

3 “Tidzaonana M’Paradaiso!”

Akhristu oona amayembekezela mwacidwi kukakhala M’paradaiso. Nkhaniyi idzafotokoza umboni wamphamvu wa M’malemba wotsimikizila kuti Paradaiso adzakhalako. Idzafotokozanso tanthauzo la mawu amene Yesu anakamba polonjeza Paradaiso.

8 Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga

9 Kodi Mukumbukila?

WIKI YA FEBRUARY 11-17, 2019

10 Muzilemekeza “Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”

Nkhaniyi idzafotokoza zimene Baibo imakamba ponena za cikwati colemekezeka. Tingaonetse bwanji kuti timalemekeza cikwati? Nanga tingaonetse bwanji kuti timayendela malangizo a m’Baibo pa nkhani ya cisudzulo na kupatukana?

15 Mbili Yanga—‘Yehova Waticitila Zinthu Zabwino’

WIKI YA FEBRUARY 18-24, 2019

19 Acicepele, Mlengi Wanu Amafuna Kuti Mukhale Acimwemwe

WIKI YA FEBRUARY 25, 2019–MARCH 3, 2019

24 Acicepele, Mungakhale na Umoyo Wacimwemwe

Acicepele nthawi zambili amafunika kupanga zosankha zazikulu. Mwacitsanzo, angafunike kudziikila zolinga zoti adzazikwanilitse mu umoyo. Kaŵili-kaŵili anthu amalimbikitsa acicepele kucita maphunzilo apamwamba kapena kupeza nchito yapamwamba. Koma Yehova amalangiza acicepele kuti ayenela kuika iye patsogolo mu umoyo. Nkhani ziŵilizi zidzatithandiza kuona kuti kumvela Mulungu ndiye cinthu canzelu.

29 “Wolungama Adzakondwela mwa Yehova”

32 Mlongoza Nkhani wa Magazini a 2018 a Nsanja ya Mlonda na Galamuka!

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani