LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 January tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 January tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Kuyambila na magazini ino, Nsanja ya Mlonda idzayamba kuonetsa mitu ya nkhani zatsopano, zolinganako na zimene kale zinali kutuluka m’magazini athu. Nkhanizi zipezeka pa webusaiti yathu ya, jw.org.

MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA

Mungatani kuti Musamakwiye Mopitirira Malire?

Kukwiya kungawononge thanzi lanu. Nakonso kubisa mkwiyo kungakubweletseleni mavuto. Kodi mungacite ciani kuti musamakwiye mopitilila malile mukakumana ndi zocitika zokhumudwitsa?

(Pitani ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ANTHU OKWATIRANA KOMANSO MABANJA.)

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

Misewu Ndi Imene Inali Nyumba Yanga

Antonio anali kukonda kucita zaciwawa, kuseŵenzetsa am’kolabongo, na kumwa moŵa mwaucakolwa, moti anali kuona kuti moyo wake ni wopanda phindu. Kodi n’ciani cinamuthandiza kusintha?

(Pitani ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MTENDERE KOMANSO MOYO WOSANGALALA.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani