LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 July tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 July tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw Laibulale Na Pa Jw.Org

KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

Manja a Octopus Ndi Ogometsa Kwambili

Akatswili acita cidwi na manja ofewa kwambili a octopus, ndipo aganiza zopanga makina amanja othandizila madokota popanga maopaleshoni ovuta kwambili.

(Pitani ku Chichewa pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO IMAPHUNZITSA > BAIBULO KOMANSO SAYANSI.)

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

“Ndinkadzikumbila Ndekha Manda”

Óscar amakhulupilila kuti akanapanda kuphunzila Mawu a Mulungu, sembe anafa kale. Óscar ni wa ku El Salvador, ndipo poyamba anali m’gulu la zigaŵenga. Kodi n’ciani cinam’sonkhezela kusintha khalidwe lake?

(Pitani ku Chichewa pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO IMAPHUNZITSA > MTENDERE KOMANSO MOYO WOSANGALALA.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani