LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w19 November tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
w19 November tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA

Kodi Kucita Zamatsenga Kuli na Vuto Lililonse?

Acicepele ambili amacita cidwi na za ziwanda, vipuku, na za ufiti. Amacitanso cidwi na openda nyenyezi. Kodi pangakhale mavuto otani ngati munthu amacita cidwi na zimenezi?

Pa jw.org, pitani ku Chichewa pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.

KODI MUKUDZIWA?

Zimene Asayansi Afukula Zikutsimikizila Kuti Mfumu Davide Analikodi

Anthu ena amanena kuti Mfumu Davide kunalibe ndipo nkhani yake ni yongopeka. Kodi asayansi apeza umboni wotani?

Pa jw.org, pitani ku Chichewa pa ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MBIRI KOMANSO BAIBULO > ZINTHU ZAKALE ZOSONYEZA KUTI BAIBULO NDI LOLONDOLA.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani