LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 11/12 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 12

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 12
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA NOVEMBER 12
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 11/12 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 12

MLUNGU WA NOVEMBER 12

Nyimbo 66 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 15 ndime 1-7, ndi bokosi patsamba 116 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Amosi 1-9 (Mph. 10)

Na. 1: Amosi 3:1-15 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi “Cipangano Catsopano” Cimanena Kuti Dziko Lapansi Lidzakhala Paladaiso Ngati Mmene “Cipangano Cakale” Cimanenela?—rs tsa. 336 ndime 1-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Kumvetsa Bwino Lemba la Salimo 51:17 Kungatithandize Bwanji? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 68

Mph. 10: Ngati Wina Anena Kuti, ‘Simumakhulupilila Yesu.’ Kukambilana kozikidwa pa buku la Kukambitsilana tsamba 433 ndime 1-3. Citani citsanzo cacidule.

Mph. 10: Kodi Tiphunzilapo Ciani? Kukambilana. Lemba ili liŵelengedwe: Maliko 1:16-20. Kambilanani mmene nkhani ili pa lembali ingatithandizile muulaliki.

Mph. 10: “Sangalalani Ndi Nchito Yanu Yakhama” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo 98 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani