LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 10
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Tumitu
  • MLUNGU WA DECEMBER 10
Utimiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa December 10

MLUNGU WA DECEMBER 10

Nyimbo 32 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 16 ndime 1-7, ndi bokosi patsamba 128 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Zefaniya 1–Hagai 2 (Mph. 10)

Na. 1: Hagai 1:1-13 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Anthu Anayamba Bwanji Kutsatila Nzelu za Anthu?—rs tsa.137 ndime 1-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kukhala ndi Maganizo a Kristu Kumatithandiza Kudziŵa Kwambili Yehova—Mat. 11:27 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 107

Mph. 15: Sukulu ya Ulaliki ya 2013. Nkhani yokambidwa ndi woyang’anila sukulu. Kambitsilanani mfundo zimene zingapindulitse mpingo wanu mwa kugwilitsila nchito malangizo a Sukulu ya Ulaliki ya 2013. Limbikitsani onse kuti aziyesetsa kukwanilitsa mbali zao, kutengako mbali pa mfundo zazikulu, ndi kugwilitsila nchito malingalilo opelekedwa mlungu uliwonse a mu buku la Sukulu ya Utumiki.

Mph. 15: “Khalani Mwamtendele ndi Anthu Onse.” Mafunso ndi mayankho. Khalani ndi zitsanzo ziŵili zacidule. Coyamba cionetse wofalitsa ayankha mwaukali mwininyumba amene alankhula naye mokwiya, ndipo caciŵili wofalitsa ayankha mofatsa.

Nyimbo 39 ndi pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani