LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 2/13 tsa. 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 11
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA FEBRUARY 11
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 2/13 tsa. 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 11

MLUNGU WA FEBRUARY 11

Nyimbo 106 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 18 ndime 18-24 (Mph.30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Mateyu 26-28 (Mph.10)

Na. 1: Mat. 27:24-44 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Kuleza Mtima Kwa Mulungu Kukuthandiza Bwanji Kuti Anthu Adzapulumuke?—2 Pet. 3:9, 15 (Mph. 5)

Na. 3: Ngati wina wanena kuti, ‘Mumakonda Kunena Kwambili za Maulosi’—rs tsa 390 ndime8–tsa. 391 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 31

Mph. 10: Tiphunzilapo Ciani? Ŵelengani Mateyu 6:19-21; Luka 16:13 ndipo kambilanani mmene malembawa angatithandizile mu utumiki.

Mph. 20: “Kodi Mudzacitako Upainiya Wothandiza?” Mafunso ndi mayankho. Ikambidwe ndi woyang’anila utumiki. Pambuyo pokambilana ndime 2, mwacidule funsani ofalitsa aŵili amene afuna kucitako upainiya wothandiza m’mwezi wa March, wina akhale wolembedwa nchito ndipo winayo akhale amene sacita zambili mu utumiki kaamba ka vuto la thanzi. Afunseni makonzedwe amene apanga kuti adzaciteko upainiya. Pambuyo pokambilana ndime 3, khalani ndi citsanzo coonetsa Akristu aŵili okwatilana kapena banja limene lili ndi ana, likucita Kulambila kwa Pabanja kuti lipange makonzedwe a mmene angafutukulile utumiki wao.

Nyimbo 122 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani