LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/13 tsa. 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 25

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 25
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 25
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 3/13 tsa. 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 25

MLUNGU WA MARCH 25

Nyimbo 76 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 20 ndime 16-20 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Luka 4–6 (Mph. 10)

Na. 1: Luka 4:22-39 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Mitundu ya Anthu Inacokela Kuti?—rs tsa 234 ndime 2-tsa 235 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Pali Umboni Wotani Wosonyeza Kuti Yesu Anaukitsidwa?—1 Akor. 15:3-7 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 111

Mph. 5: Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu Coyamba mu April. Mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo uli patsamba 8, onetsani mmene tingayambitsile phunzilo pa Ciŵelu coyamba mu April. Limbikitsani onse kutengako mbali.

Mph. 25: “Mmene mungagwilitsile nchito kabuku kakuti Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu!” Mafunso ndi mayankho. Pokambilana ndime 6, citani zitsanzo ziŵili.

Nyimbo 97 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani