Ndandanda ya Mlungu wa March 25
MLUNGU WA MARCH 25
Nyimbo 76 ndi Pemphelo
□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:
bt mutu 20 ndime 16-20 (Mph. 30)
□ Sukulu ya Ulaliki:
Kuŵelenga Baibo: Luka 4–6 (Mph. 10)
Na. 1: Luka 4:22-39 (Mph. 4 kapena zocepelapo)
Na. 2: Kodi Mitundu ya Anthu Inacokela Kuti?—rs tsa 234 ndime 2-tsa 235 ndime 1 (Mph. 5)
Na. 3: Kodi Pali Umboni Wotani Wosonyeza Kuti Yesu Anaukitsidwa?—1 Akor. 15:3-7 (Mph. 5)
□ Msonkhano wa Nchito:
Nyimbo 111
Mph. 5: Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu Coyamba mu April. Mwa kugwilitsila nchito ulaliki wacitsanzo uli patsamba 8, onetsani mmene tingayambitsile phunzilo pa Ciŵelu coyamba mu April. Limbikitsani onse kutengako mbali.
Mph. 25: “Mmene mungagwilitsile nchito kabuku kakuti Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu!” Mafunso ndi mayankho. Pokambilana ndime 6, citani zitsanzo ziŵili.
Nyimbo 97 ndi Pemphelo