LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 17

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 17
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 17
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa March 17

MLUNGU WA MARCH 17

Nyimbo 113 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 6 ndime 1-6 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Genesis 43-46 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 44:18-34 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Ndi Anthu Enanso Ati Amene Adzaukitsidwa Kuti Akhale Ndi Moyo Padziko Lapansi?—rs tsa. 113 ndime 1-5 (Mph. 5)

Na. 3: N’cifukwa Ciani Tiyenela Kupitiliza Kudalila Yehova?—bh tsa. 164 mpaka 165 ndime 1-4 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 61

Mph. 15: Khalani Osamala Polalikila. Nkhani yokambitsilana yocokela m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 197, ndime 1, mpaka tsamba 199, ndime 4. Citani citsanzo coonetsa wofalitsa akuyankha mosasamala munthu wotsutsa. Kenako citani citsanzo cina coonetsa wofalitsa akuyankha mosamala kwambili munthu wotsutsa.

Mph. 15: “Kodi Mudzatengako Mbali?” Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvela kuti afotokoze mmene aziŵelengela Malemba amene asankhidwa panyengo ya Cikumbutso. Fotokozani zimene mwakonza kucita pampingo wanu panyengo ya Cikumbutso.

Nyimbo 8 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani