LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsa. 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 20

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 20
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA OCTOBER 20
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsa. 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 20

MLUNGU WA OCTOBER 20

Nyimbo 109 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 15 ndime 1 mpaka 6, ndi bokosi patsamba 184 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: Deuteronomo 7-10 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 9:15-29 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Cifukwa Cake Zinali Zotheka Kuti Munthu Wangwilo Acimwe—rs tsa. 358 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Tisamakaikile Zimene Yehova Wasankha—(Aroma 11:33, 1 Yoh. 4:8 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 116

Mph. 15: “Kufotokoza Zimene Timakhulupilila Zokhudza 1914.” Kukambilana. Pemphani omvela kuti akambepo pa funso lililonse lili ndi kadontho kakuda.

Mph. 15: Cida Cimene Cingatithandize Kufotokoza Zimene Timakhulupilila Zokhudza 1914. Yambani ndi citsanzo ca mphindi 7 coonetsa wofalitsa akugwilitsila nchito chati cimene cili pa tsamba 216 mʼbuku lakuti Zimene Baibo Limaphunzitsa. Wofalitsayo akuthandiza Phunzilo la Baibulo kuona mmene ulosi wolembedwa mu Danieli caputala 4 umagwilizanilana ndi Ufumu wa Mulungu. Pemphani omvela kufotokoza cifukwa cake citsanzoci ndi cothandiza. Tsilizani mwa kuŵelenga Chivumbulutso 12:10, 12. Ndiyeno, pemphani omvela kufotokoza cifukwa cake kudziŵa kuti Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulila mu 1914 kumatilimbikitsa kulalikila mwacangu.

Nyimbo 133 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani