LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsa. 4
  • Zilengezo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zilengezo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsa. 4

Zilengezo

◼ Cogaŵila ca mu October: Magazini a Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani! November ndi December: Gaŵilani buku la mutu wakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni kapena gaŵilani kalikonse ka tumapepala twauthenga utu: Kodi Baibo Mumaiona Bwanji?, Kodi Zinthu Zidzakhala Bwanji Mtsogolo?, Kodi Cofunika N’ciani Kuti Banja Likhale Lamtendele?, Kodi Ndani Maka-maka Amene Akulamulila Dzikoli?, Kodi Mavuto Adzathadi?, ndi kakuti Kodi N’zoona Kuti Akufa Angakhalenso ndi Moyo? January: Gaŵilani kabuku kakuti, Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu.

◼ Ndife osangalala kuti m’caka cautumiki cino mpaka mwezi wa June, mipingo yatsopano yokwana 96 inapangidwa, ndipo Nyumba za Ufumu zatsopano zoposa 32 zinamangidwa.

◼ Galamukani! ya Cikikaonde idzayamba kutuluka kamodzi pamwezi, kuyambila ndi ya November 2014.

◼ Tikuyamikilani cifukwa colemba lipoti la zimene munagaŵila mu ulaliki wakumunda. M’mwezi wa March tinagaŵila tumabuku ndi tumapepala twauthenga toposa 892,000, cimeneci ndi ciŵelengelo capamwamba kuposa kale lonse.

◼ Ndife okondwa kukudziŵitsani kuti buku lakuti Khalanibe m’Cikondi ca Mulungu, tsopano likupezeka m’cinenelo ca Cimambwe-Lungu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani