LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 3/15 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 30

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 30
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MARCH 30
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 3/15 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa March 30

MLUNGU WA MARCH 30

Nyimbo 57 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 7 ndime 9-17 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Samueli 14–15 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 14:36-45 (Mph. 3 kapena zocepelapo)

Na. 2: Balamu—Mutu: Mtima Wadyela Ungatipangitse Kucita Zinthu Zoipa—(lv nkhani 9 tsa. 97 ndime 2) (Mph. 5)

Na. 3: Kukwanilitsidwa kwa Maulosi a m’Baibulo Okhudza Masiku Otsiliza—igw-CIN tsa. 13 (Mph. 5)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: ‘Khalani Okonzeka Kugwila Nchito Iliyonse Yabwino.’—Tito 3:1.

Nyimbo 37

Mph. 15: Mavidiyo Ena a pa Webusaiti Yathu Amene Tingagwilitsile Nchito mu Ulaliki. Kukambilana. Yambani mwa kuonetsa vidiyo yakuti, Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji? Ndiyeno kambilanani mmene mungagwilitsile nchito vidiyo imeneyi mu ulaliki. Citaninso cimodzimodzi ndi vidiyo yakuti, N’ciani Cimacitika ku Nyumba ya Ufumu? Phatikizanipo citsanzo. Ngati n’zosatheka kuonelela vidiyo, kambilanani nkhani yakuti “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki” imene ili mu Utumiki Wathu wa Ufumu wa December 2014, tsamba 1.

Mph. 15: “Gwilitsilani Nchito Kabuku Kakuti, Mfundo za m’Mau a Mulungu—Poyambitsa Makambilano.” Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvela kuti anene mmene angagwilitsile nchito kabuku kakuti, Mfundo za m’Mau a Mulungu mu ulaliki. Citani citsanzo.

Nyimbo 114 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani